Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 20:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Koma izi zalembedwa+ kuti mukhulupirire kuti Yesu alidi Khristu Mwana wa Mulungu, ndi kutinso, mwa kukhulupirira,+ mukhale ndi moyo m’dzina lake.

  • Yohane 21:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Wophunzira ameneyu+ ndiye akuchitira umboni zinthu zimenezi. Iyeyu ndi amenenso analemba zinthu zimenezi, ndipo tikudziwa kuti umboni umene akupereka ndi woona.+

  • 1 Yohane 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Tikukulemberani za iye amene analiko kuyambira pa chiyambi,+ amene amabweretsa mawu opatsa moyo,+ amene tamumva+ ndiponso kumuona ndi maso athu,+ amene tamuyang’anitsitsa+ mwachidwi ndi kumukhudza ndi manja athu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena