Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 6:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Koma anthu anawaona akuchoka ndipo ambiri anadziwa zimenezo. Chotero kuchokera m’mizinda yonse, anthu anathamangira kumeneko wapansi, ndipo anthuwo ndi amene anayamba kukafika kumaloko.+

  • Luka 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma khamu la anthu linadziwa ndi kum’tsatira. Iye anawalandirabe bwino ndi kuyamba kuwauza za ufumu wa Mulungu,+ ndipo anachiritsa amene anafunika kuchiritsidwa.+

  • Yohane 2:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Tsopano pamene anali mu Yerusalemu pa chikondwerero+ cha pasika, anthu ambiri anakhulupirira m’dzina lake,+ ataona zizindikiro zimene anali kuchita.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena