15 Ndidzaika+ chidani+ pakati pa iwe+ ndi mkaziyo,+ ndi pakati pa mbewu yako+ ndi mbewu yake.+ Mbewu ya mkaziyo+ idzaphwanya mutu wako,+ ndipo iwe+ udzaivulaza chidendene.”+
10 n’kunena kuti: “Iwe munthu wodzazidwa ndi mtundu uliwonse wa chinyengo ndi zoipa, mwana wa Mdyerekezi,+ mdani wa chilichonse cholungama, kodi sudzaleka kupotoza njira zowongoka za Yehova?