Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 12:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mawu a Yehova ndi oyengeka bwino,+

      Ngati siliva woyengedwa nthawi zokwanira 7 mung’anjo ya m’nthaka.

  • Salimo 119:151
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 151 Inu Yehova muli pafupi,+

      Ndipo malamulo anu onse ndi choonadi.+

  • Salimo 119:160
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 160 Mawu anu onse ndi choonadi chokhachokha,+

      Ndipo chigamulo chanu chilichonse cholungama chidzakhalapo mpaka kalekale.+

  • Yakobo 1:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pakuti mwa chifuniro+ chake, iye anatibala ife ndi mawu a choonadi.+ Anachita zimenezi kuti tikhale zipatso zoyambirira+ pa zolengedwa zake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena