Mateyu 28:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Koma ophunzira 11 aja anapita ku Galileya,+ kuphiri kumene Yesu anakonza kukakumana nawo. Machitidwe 1:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndiponso, mwa maumboni ambiri otsimikizika, iye anadzionetsa kwa atumwiwo kuti ali moyo pambuyo pa zovuta zimene anakumana nazo.+ Iwo anamuona masiku onse 40, ndipo anali kuwauza za ufumu wa Mulungu.+ Machitidwe 3:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Chotero munapha Mtumiki Wamkulu wa moyo,+ koma Mulungu anamuukitsa kwa akufa, ndipo ife ndife mboni za choonadi chimenechi.+ 1 Akorinto 15:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndiyeno anaonekeranso kwa abale oposa 500 pa nthawi imodzi, ndipo ambiri a iwo akali ndi moyo mpaka lero,+ koma ena anagona mu imfa.
3 Ndiponso, mwa maumboni ambiri otsimikizika, iye anadzionetsa kwa atumwiwo kuti ali moyo pambuyo pa zovuta zimene anakumana nazo.+ Iwo anamuona masiku onse 40, ndipo anali kuwauza za ufumu wa Mulungu.+
15 Chotero munapha Mtumiki Wamkulu wa moyo,+ koma Mulungu anamuukitsa kwa akufa, ndipo ife ndife mboni za choonadi chimenechi.+
6 Ndiyeno anaonekeranso kwa abale oposa 500 pa nthawi imodzi, ndipo ambiri a iwo akali ndi moyo mpaka lero,+ koma ena anagona mu imfa.