Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Wopusa amanena mumtima mwake kuti:

      “Kulibe Yehova.”+

      Anthu oterewa amachita zoipa,+ ndipo amachita zinthu zonyansa.

      Palibe amene akuchita zabwino.+

  • Miyambo 20:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndani anganene kuti: “Ndayeretsa mtima wanga,+ ndadziyeretsa ku tchimo langa”?+

  • Mlaliki 7:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Palibe munthu wolungama padziko lapansi amene amachita zabwino zokhazokha osachimwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena