Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Akorinto 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inunso mungathandizepo mwa kutiperekera mapembedzero anu,+ kuti pakhale anthu ambiri otiperekera mapemphero oyamikira+ zinthu zimene tapatsidwa mokoma mtima, chifukwa cha mapemphero a anthu ambiri.+

  • Aefeso 6:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pamene mukutero, muzipemphera pa chochitika chilichonse mu mzimu,+ mwa mtundu uliwonse wa pemphero+ ndi pembedzero. Kuti muchite zimenezi, khalani maso mosalekeza ndi kupemphera mopembedzera m’malo mwa oyera onse,

  • Akolose 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Muzitipemphereranso ifeyo,+ kuti Mulungu atitsegulire khomo+ kuti tithe kulalikira mawu ndi kulankhula za chinsinsi chopatulika+ chonena za Khristu, chimene ndinamangidwira n’kukhala m’ndende muno,+

  • 1 Atesalonika 5:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Abale, pitirizani kutipempherera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena