1 Akorinto 10:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 monga mmene ineyo ndikukondweretsera anthu onse m’zinthu zonse.+ Sikuti ndikungofuna zopindulitsa ine ndekha ayi,+ koma zopindulitsa anthu ambiri, kuti apulumutsidwe.+ 1 Akorinto 13:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 sichichita zosayenera,+ sichisamala zofuna zake zokha,+ sichikwiya.+ Sichisunga zifukwa.+ Afilipi 2:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Pakuti ena onse akungofuna za iwo eni,+ osati za Khristu Yesu.
33 monga mmene ineyo ndikukondweretsera anthu onse m’zinthu zonse.+ Sikuti ndikungofuna zopindulitsa ine ndekha ayi,+ koma zopindulitsa anthu ambiri, kuti apulumutsidwe.+