Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 101:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 M’nyumba yanga simudzakhala wochita chinyengo.+

      Ndipo aliyense wolankhula zachinyengo sadzapitiriza kukhala+

      Pamaso panga.+

  • Salimo 119:118
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 118 Onse osochera ndi kuchoka pa malangizo anu mwawataya kutali,+

      Pakuti ndi achinyengo komanso onama.+

  • Machitidwe 5:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Petulo anati: “Hananiya, n’chifukwa chiyani Satana+ wakulimbitsa mtima choncho kuti uyese kunamiza+ mzimu woyera+ ndi kubisa zina mwa ndalama za mtengo wa mundawo?

  • Aefeso 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Inde, kuti tisakhalenso tiana, otengekatengeka+ ngati kuti tikukankhidwa ndi mafunde, ndiponso otengeka kupita uku ndi uku ndi mphepo iliyonse ya chiphunzitso+ chonyenga+ cha anthu, mwa kuchenjera kwa anthu popeka mabodza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena