Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 38:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Tsopano Yehova analankhula+ ndi Yesaya kuti:

  • Machitidwe 8:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Choncho atatha kuchitira umboni mokwanira ndi kulankhula mawu a Yehova, anabwerera ku Yerusalemu. Pamene anali kubwerera anali kulengeza uthenga wabwino m’midzi yambiri ya Asamariya.+

  • Machitidwe 15:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Koma Paulo ndi Baranaba anatsalira ku Antiokeya.+ Ndipo iwo pamodzi ndi enanso ambiri anali kuphunzitsa ndi kulengeza uthenga wabwino wa mawu a Yehova.+

  • 1 Atesalonika 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndipotu, si kuti mawu a Yehova+ ochokera kwa inu amveka ku Makedoniya ndi ku Akaya kokha ayi, koma kwina kulikonse chikhulupiriro+ chanu mwa Mulungu chafalikira,+ moti ife sitikufunika kunenapo kanthu.

  • 1 Petulo 1:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 koma mawu a Yehova amakhala kosatha.”+ “Mawu”+ amenewo ndi amene alengezedwa+ kwa inu monga uthenga wabwino.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena