Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 8:14-17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Atatero anabweretsa ngʼombe yamphongo ya nsembe yamachimo ndipo Aroni ndi ana ake anaika manja awo pamutu pa ngʼombe ya nsembe yamachimoyo.+ 15 Ndiyeno Mose anapha ngʼombeyo nʼkutenga magazi+ ndi chala chake ndipo anawapaka panyanga zonse za guwa lansembe nʼkuyeretsa guwalo ku uchimo. Koma magazi otsalawo anawathira pansi pa guwa lansembe kuti alipatule, kuphimba machimo paguwalo. 16 Atatero Mose anatenga mafuta onse okuta matumbo, mafuta apachiwindi, impso ziwiri ndi mafuta ake, nʼkuziwotcha paguwa lansembe.+ 17 Koma ngʼombe yonseyo, chikopa chake, nyama yake ndi ndowe zake anaziwotcha pamoto kunja kwa msasa,+ mogwirizana ndi zimene Yehova analamula Mose.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena