Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • bi12 tsamba 1960-1967
  • 21 Zochitika Zazikulu M’moyo wa Yesu Padziko Lapansi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • 21 Zochitika Zazikulu M’moyo wa Yesu Padziko Lapansi
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Timitu
  • Zochitika Zotifikitsa pa Nthawi ya Utumiki wa Yesu
  • Chiyambi cha Utumiki wa Yesu
  • Utumiki Waukulu wa Yesu m’Galileya
  • Utumiki wa Yesu Wakumapeto mu Yudeya
  • Utumiki wa Yesu Wakumapeto Kum’mawa kwa Yorodano
  • Utumiki Womaliza wa Yesu m’Yerusalemu
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
21 Zochitika Zazikulu M’moyo wa Yesu Padziko Lapansi

21 Zochitika Zazikulu M’moyo wa Yesu Padziko Lapansi

Zochitika za m’Mauthenga Abwino Anayi, Zondandalikidwa Motsatira Nthawi Imene Zinachitika

Zochitika Zotifikitsa pa Nthawi ya Utumiki wa Yesu

NTHAWI

MALO

CHOCHITIKA

LEMBA

3 B.C.E.

Yerusalemu, m’kachisi

Zekariya auzidwiratu za kubadwa kwa Yohane M’batizi

Luka 1:5-25

c. 2 B.C.E.

Nazareti, ku Yudeya

Mariya auzidwiratu za kubadwa kwa Yesu, ndipo achezera Elizabeti

Luka 1:26-56

2 B.C.E.

Dera la kumapiri la Yudeya

Kubadwa kwa Yohane M’batizi. Pambuyo pake, moyo wake m’chipululu

Luka 1:57-80

2 B.C.E., c. Oct. 1

Betelehemu

Kubadwa kwa Yesu (Mawuyo, amene zinthu zonse zinakhalako kudzeramwa iye) monga mbadwa ya Abulahamu ndi ya Davide

Mateyu 1:1-25

Luka 2:1-7

Yohane 1:1-5, 9-14

Pafupi ndi Betelehemu

Mngelo alengeza nkhani yabwino.Abusa apita kukaona mwana wakhandayo

Luka 2:8-20

Betelehemu, Yerusalemu

Yesu adulidwa (tsiku la 8), aperekedwa m’kachisi (tsiku la 40)

Luka 2:21-38

1 B.C.E. kapena 1 C.E.

Yerusalemu, Betelehemu, Nazareti

Okhulupirira nyenyezi. Athawira ku Iguputo. Ana akhanda aphedwa. Yesu abwerera

Mateyu 2:1-23

Luka 2:39, 40

12 C.E.

Yerusalemu

Yesu wa zaka 12 pa chikondwerero cha Pasika. Apita kunyumba

Luka 2:41-52

29, chakumayambiriro kwa chaka

Chipululu, Yorodano

Utumiki wa Yohane M’batizi

Mateyu 3:1-12

Maliko 3:1-18

Luka 3:1-18

Yohane 1:6-8, 15-28

Chiyambi cha Utumiki wa Yesu

NTHAWI

MALO

CHOCHITIKA

LEMBA

29, chakumapeto kwa chaka

Mtsinje wa Yorodano

Ubatizo ndi kudzozedwa kwa Yesu, wobadwa monga munthu mu mzera wa Davide, koma wolengezedwa kukhala Mwana wa Mulungu

Mateyu 3:13-17

Maliko 1:9-11

Luka 3:21-38

Yohane 1:32-34

Chipululu cha Yudeya

Yesu asala kudya ndipo ayesedwa

Mateyu 4:1-11

Maliko 1:12, 13

Luka 4:1-13

Betaniya wa kutsidya lina la Yorodano

Umboni wa Yohane M’batizi wonenaza Yesu

Yohane 1:15, 29-34

Kumtunda kwa chigwa cha Yorodano

Ophunzira oyamba a Yesu

Yohane 1:35-51

Kana wa ku Galileya, Kaperenao

Chozizwitsa choyamba cha Yesu. Apita ku Kaperenao

Yohane 2:1-12

30, Pasika

Yerusalemu

Kuchita Pasika. Athamangitsa amalonda m’kachisi

Yohane 2:13-25

Yerusalemu

Yesu akambirana ndi Nikodemo

Yohane 3:1-21

Yudeya, Ainoni

Ophunzira a Yesu abatiza anthu. Yohane azicheperachepera

Yohane 3:22-36

Tiberiyo

Yohane aponyedwa m’ndende. Yesu anyamuka kupita ku Galileya

Mateyu 4:12; 14:3-5

Maliko 1:14; 6:17-20

Luka 3:19, 20; Luka 4:14

Yohane 4:1-3

Sukari, ku Samariya

Pa ulendo wa ku Galileya, Yesu aphunzitsa Asamariya

Yohane 4:4-43

Utumiki Waukulu wa Yesu m’Galileya

NTHAWI

MALO

CHOCHITIKA

LEMBA

30, Pasika

Galileya

Choyamba alengeza kuti, “Ufumu wakumwamba wayandikira”

Mateyu 4:17

Maliko 1:14, 15

Luka 4:14, 15

Yohane 4:44, 45

Nazareti, Kana, Kaperenao

Achiritsa mnyamata, awerenga za ntchito yake, akanidwa, apita ku Kaperenao

Mateyu 4:13-16

Luka 4:16-31

Yohane 4:46-54

Nyanja ya Galileya, pafupi ndi Kaperenao

Kuitanidwa kwa Simoni ndi Andireya, Yakobo ndi Yohane

Mateyu 4:18-22

Maliko 1:16-20

Luka 5:1-11

Kaperenao

Achiritsa waziwanda, apongozi a Petulo, ndi enanso ambiri

Mateyu 8:14-17

Maliko 1:21-34

Luka 4:31-41

Galileya

Ulendo woyamba wozungulira mu Galileya, ali ndi ophunzira anayi oitanidwa kumene

Mateyu 4:23-25

Maliko 1:35-39

Luka 4:42, 43

Galileya

Wakhate achiritsidwa, anthu miyandamiyanda akhamukira kwa Yesu

Mateyu 8:1-4

Maliko 1:40-45

Luka 5:12-16

Kaperenao

Achiritsa wakufa ziwalo

Mateyu 9:1-8

Maliko 2:1-12

Luka 5:17-26

Kaperenao

Kuitanidwa kwa Mateyu. Achita phwando ndi okhometsa msonkho

Mateyu 9:9-17

Maliko 2:13-22

Luka 5:27-39

Yudeya

Alalikira m’masunagoge a ku Yudeya

Luka 4:44

31, Pasika

Yerusalemu

Achita nawo phwando, achiritsa mwamuna wina, adzudzula Afarisi

Yohane 5:1-47

Kubwerera kuchokera ku Yerusalemu(?)

Ophunzira abudula ngala za tirigu pa Sabata

Mateyu 12:1-8

Maliko 2:23-28

Luka 6:1-5

Galileya, nyanja ya Galileya

Achiritsa dzanja pa Sabata, apita kukapumula kugombe la nyanja, achiritsa anthu

Mateyu 12:9-21

Maliko 3:1-12

Luka 6:6-11

Phiri la pafupi ndi Kaperenao

Anthu 12 asankhidwa kukhala atumwi

Maliko 3:13-19

Luka 6:12-16

Pafupi ndi Kaperenao

Ulaliki wa paphiri

Mateyu 5:1–7:29

Luka 6:17-49

Kaperenao

Achiritsa wantchito wa kapitawo wa asilikali

Mateyu 8:5-13

Luka 7:1-10

Naini

Aukitsa mwana wa mkazi wamasiye

Luka 7:11-17

Galileya

Yohane m’ndende atumiza ophunzira ake kwa Yesu

Mateyu 11:2-19

Luka 7:18-35

Galileya

Mizinda idzudzulidwa, kuululira zinthu tiana, goli lofewa

Mateyu 11:20-30

Galileya

Mzimayi wochimwa athira mafuta pamapazi ake, fanizo la anthu angongole

Luka 7:36-50

Galileya

Ulendo wachiwiri wolalikira m’Galileya, limodzi ndi atumwi 12

Luka 8:1-3

Galileya

Waziwanda achiritsidwa, Yesu akum’neneza kuti ndi wogwirizana ndi Belezebule

Mateyu 12:22-37

Maliko 3:19-30

Galileya

Alembi ndi Afarisi afuna kuona chizindikiro

Mateyu 12:38-45

Galileya

Ophunzira a Khristu ndiwo achibale ake enieni

Mateyu 12:46-50

Maliko 3:31-35

Luka 8:19-21

Nyanja ya Galileya

Mafanizo a wofesa mbewu, namsongole, ndi ena. Mafotokozedwe ake

Mateyu 13:1-53

Maliko 4:1-34

Luka 8:4-18

Nyanja ya Galileya

Podutsa nyanja aimitsa mphepo yamkuntho

Mateyu 8:18, 23-27

Maliko 4:35-41

Luka 8:22-25

Gadara, Kum’mwera chakum’mawa ya nyanja ya Galileya

Aziwanda awiri achiritsidwa, nkhumba zigwidwa ndi ziwanda

Mateyu 8:28-34

Maliko 5:1-20

Luka 8:26-39

Mwina ku Kaperenao

Mwana wamkazi wa Yairo aukitsidwa, mkazi achiritsidwa

Mateyu 9:18-26

Maliko 5:21-43

Luka 8:40-56

Kaperenao(?)

Achiritsa amuna awiri akhungu ndi waziwanda wosalankhula

Mateyu 9:27-34

Nazareti

Achezeranso mzinda umene anakulirako ndipo akanidwanso

Mateyu 13:54-58

Maliko 6:1-6

Galileya

Ulendo wachitatu woyendera Galileya, madera ambiri ayenderedwa iye atatumiza atumwi

Mateyu 9:35–11:1

Maliko 6:6-13

Luka 9:1-6

Tiberiyo

Yohane M’batizi adulidwa mutu, mantha a Herode chifukwa cha mlanduwo

Mateyu 14:1-12

Maliko 6:14-29

Luka 9:7-9

32, chikondwerero cha Pasika chitayandikira (Yoh 6:4)

Kaperenao(?), Kumpoto chakum’mawa kwa nyanja ya Galileya

Atumwi abwerako pa ulendo wokalalikira, 5,000 adyetsedwa

Mateyu 14:13-21

Maliko 6:30-44

Luka 9:10-17

Yohane 6:1-13

Kumpoto chakum’mawa kwa nyanja ya Galileya, Genesarete

Ayesa kulonga Yesu ufumu, ayenda panyanja, achiritsa anthu

Mateyu 14:22-36

Maliko 6:45-56

Yohane 6:14-21

Kaperenao

Afotokoza za “chakudya chopatsamoyo,” ophunzira ambiri asiya kum’tsatira

Yohane 6:22-71

32, pambuyo pa Pasika

Mwina ku Kaperenao

Miyambo yochititsa Mawu a Mulungu kukhala opanda pake

Mateyu 15:1-20

Maliko 7:1-23

Luka 7:1

Foinike,

Pafupi ndi Turo, Sidoni. Kenako ku Dekapole, 4,000 adyetsedwa

Mateyu 15:21-38

Maliko 7:24–8:9

Magadani

Asaduki ndi Afarisi afunanso chizindikiro

Mateyu 15:39–16:4

Maliko 8:10-12

Kumpoto chakum’mawa kwa nyanja ya Galileya, Betsaida

Achenjeza za chofufumitsa cha Afarisi, achiritsa wakhungu

Mateyu 16:5-12

Maliko 8:13-26

Kaisareya wa Filipi

Yesu Mesiya, aneneratu za imfa yake, kuukitsidwa

Mateyu 16:13-28

Maliko 8:27–9:1

Luka 9:18-27

Mwina phiri la Herimoni

Kusandulika pamaso pa Petulo, Yakobo, ndi Yohane

Mateyu 17:1-13

Maliko 9:2-13

Luka 9:28-36

Kaisareya wa Filipi

Achiritsa waziwanda amene ophunzira alephera kum’chiritsa

Mateyu 17:14-20

Maliko 9:14-29

Luka 9:37-43

Galileya

Aneneratunso za imfa yake ndi kuukitsidwa kwake

Mateyu 17:22, 23

Maliko 9:30-32

Luka 9:43-45

Kaperenao

Ndalama yokakhomera msonkho iperekedwa mozizwitsa

Mateyu 17:24-27

Kaperenao

Wamkulu koposa mu Ufumu. Kukambirana zolakwa, chifundo

Mateyu 18:1-35

Maliko 9:33-50

Luka 9:46-50

Galileya, Samariya

Anyamuka ku Galileya apita ku Chikondwerero cha Misasa. Zonse azipatulira utumiki

Mateyu 8:19-22

Luka 9:51-62

Yohane 7:2-10

Utumiki wa Yesu Wakumapeto mu Yudeya

NTHAWI

MALO

CHOCHITIKA

LEMBA

32, Chikondwerero cha Misasa

Yerusalemu

Yesu aphunzitsa anthu pa Chikondwerero cha Misasa

Yohane 7:11-52

Yerusalemu

Kuphunzitsa pambuyo pa Chikondwererocho, achiritsa akhungu

Yohane 8:12–9:41

Mwina ku Yudeya

Atumwi 70 atumizidwa kukalalikira, abwerako, apereka lipoti

Luka 10:1-24

Yudeya, Betaniya

Afotokoza za Msamariya wachifundo. Panyumba ya Malita, Mariya

Luka 10:25-42

Mwina ku Yudeya

Aphunzitsanso pemphero lachitsanzo. Kulimbikira kupempha

Luka 11:1-13

Mwina ku Yudeya

Akana mlandu womunamizira. Asonyeza kuti m’badwowo ndi woyenera chilango

Luka 11:14-36

Mwina ku Yudeya

Pa chakudya kwa Mfarisi, Yesu adzudzula achinyengo

Luka 11:37-54

Mwina ku Yudeya

Akamba nkhani ya mmene Mulungu Amatisamalira. Mtumiki woyang’anira nyumba wokhulupirika

Luka 12:1-59

Mwina ku Yudeya

Achiritsa mkazi wolumala pa Sabata, mafanizo atatu

Luka 13:1-21

32, Chikondwerero cha Kupereka Kachisi kwa Yesu pa Mulungu

Yerusalemu

Chikondwerero cha Kupereka Kachisi kwa Mulungu. M’busa Wabwino

Yohane 10:1-39

Utumiki wa Yesu Wakumapeto Kum’mawa kwa Yorodano

NTHAWI

MALO

CHOCHITIKA

LEMBA

32, Chikondwerero cha Kupereka Kachisi kwa Yesu pa Mulungu

Tsidya la Yorodano

Ambiri akhulupirira Yesu

Yohane 10:40-42

Pereya (kutsidya la Yorodano)

Aphunzitsa m’mizinda, m’midzi, alowera ku Yerusalemu

Luka 13:22

Pereya

Kulowa mu Ufumu, Herode aopseza, nyumba yabwinja

Luka 13:23-35

Mwina ku Pereya

Kudzichepetsa, fanizo la phwando lalikulu la chakudya chamadzulo

Luka 14:1-24

Mwina ku Pereya

Kuwerengera mtengo wa kukhala wophunzira

Luka 14:25-35

Mwina ku Pereya

Mafanizo: nkhosa yotayika, ndalama yotayika, mwana wolowerera

Luka 15:1-32

Mwina ku Pereya

Mafanizo: mtumiki woyang’anira nyumba wosalungama, munthu wolemera ndi Lazaro

Luka 16:1-31

Mwina ku Pereya

Kukhululukira ndi chikhulupiriro, akapolo opanda pake

Luka 17:1-10

Betaniya

Lazaro aukitsidwa kwa akufa ndi Yesu

Yohane 11:1-46

Yerusalemu, Efuraimu

Uphungu wa Kayafa kuti Yesu aphedwe, Yesu achokako

Yohane 11:47-54

Samariya, Galileya

Achiritsa ndi kuphunzitsa anthu pa ulendo wake wodutsa m’Samariya, Galileya

Luka 17:11-37

Samariya kapena Galileya

Mafanizo: mkazi wamasiye wolimbikira kupempha, Mfarisi ndi wokhometsa msonkho

Luka 18:1-14

Pereya

Adutsa m’Pereya, aphunzitsa za kuthetsa ukwati

Mateyu 19:1-12

Maliko 10:1-12

Pereya

Alandira ndi kudalitsa ana aang’ono

Mateyu 19:13-15

Maliko 10:13-16

Luka 18:15-17

Pereya

Mwamuna wachinyamata wolemera, fanizo la antchito am’munda wa mpesa

Mateyu 19:16–20:16

Maliko 10:17-31

Luka 18:18-30

Mwina ku Pereya

Kachitatu Yesu aneneratu za imfa yake, kuukitsidwa

Mateyu 20:17-19

Maliko 10:32-34

Luka 18:31-34

Mwina ku Pereya

Kupemphera malo Yakobo ndi Yohane mu Ufumu

Mateyu 20:20-28

Maliko 10:35-45

Yeriko

Podutsa m’Yeriko achiritsa amuna awiri akhungu, achezera Zakeyu. Fanizo la ndalama 10 za mina

Mateyu 20:29-34

Maliko 10:46-52

Luka 18:35–19:28

Utumiki Womaliza wa Yesu m’Yerusalemu

NTHAWI

MALO

CHOCHITIKA

LEMBA

Nisani 8, 33

Betaniya

Afika ku Betaniya masiku 6 Pasika asanachitike

Yohane 11:55–12:1

Nisani 9

Betaniya

Phwando panyumba ya Simoni wakhate, Mariya athira mafuta Yesu, Ayuda afika kudzaona Yesu ndi Lazaro

Mateyu 26:6-13

Maliko 14:3-9

Yohane 12:2-11

Betaniya-Yerusalemu

Khristu alowa monga wopambana m’Yerusalemu

Mateyu 21:1-11, 14-17

Maliko 11:1-11

Luka 19:29-44

Yohane 12:12-19

Nisani 10

Betaniya-Yerusalemu

Mkuyu wosabala utembereredwa, kuyeretsa kachisi kachiwiri

Mateyu 21:18, 19, 12, 13

Maliko 11:12-17

Luka 19:45, 46

Yerusalemu

Ansembe aakulu ndi alembi akonza chiwembu kuti aphe Yesu

Maliko 11:18, 19

Luka 19:47, 48

Yerusalemu

Kukambirana ndi Agiriki, kusakhulupirira kwa Ayuda

Yohane 12:20-50

Nisani 11

Betaniya-Yerusalemu

Mkuyu wosabala aupeza utauma

Mateyu 21:19-22

Maliko 11:20-25

Yerusalemu, m’kachisi

Akayikira ulamuliro wa Khristu, fanizo la ana aamuna awiri

Mateyu 21:23-32

Maliko 11:27-33

Luka 20:1-8

Yerusalemu, m’kachisi

Mafanizo a olima munda oipa, phwando la ukwati

Mateyu 21:33–22:14

Maliko 12:1-12

Luka 20:9-19

Yerusalemu, m’kachisi

Mafunso ofuna kum’kola nawo pa nkhani za msonkho, kuuka kwa akufa, ndi lamulo

Mateyu 22:15-40

Maliko 12:13-34

Luka 20:20-40

Yerusalemu, m’kachisi

Funso la Yesu lowagometsa pa nkhani ya mzera wobadwiramo wa Mesiya

Mateyu 22:41-46

Maliko 12:35-37

Luka 20:41-44

Yerusalemu, m’kachisi

Adzudzula mwamphamvu alembi ndi Afarisi

Mateyu 23:1-39

Maliko 12:38-40

Luka 20:45-47

Yerusalemu, m’kachisi

Kakhobidi ka mkazi wamasiye

Maliko 12:41-44

Luka 21:1-4

Phiri la Maolivi

Aneneratu za kugwa kwa Yerusalemu, kukhalapo kwa Yesu, mapeto a nthawi ino

Mateyu 24:1-51

Maliko 13:1-37

Luka 21:5-38

Phiri la Maolivi

Mafanizo a anamwali 10, matalente, nkhosa ndi mbuzi

Mateyu 25:1-46

Nisani 12

Yerusalemu

Atsogoleri achipembedzo akonza zopha Yesu

Mateyu 26:1-5

Maliko 14:1, 2

Luka 22:1, 2

Yerusalemu

Yudasi akambirana ndi ansembe za kupereka Yesu

Mateyu 26:14-16

Maliko 14:10, 11

Luka 22:3-6

Nisani 13 (Lachinayi masana)

Pafupi ndi Yerusalemu, ndi mkati mwake

Kukonzekera Pasika

Mateyu 26:17-19

Maliko 14:12-16

Luka 22:7-13

Nisani 14

Yerusalemu

Adya chakudya cha Pasika pamodzi ndi atumwi 12

Mateyu 26:20, 21

Maliko 14:17, 18

Luka 22:14-18

Yerusalemu

Yesu asambitsa mapazi a atumwi ake

Yohane 13:1-20

Yerusalemu

Yudasi aululika kuti ndiye adzam’pereke ndipo auzidwa kuchoka

Mateyu 26:21-25

Maliko 14:18-21

Luka 22:21-23

Yohane 13:21-30

Yerusalemu

Chakudya chamadzulo cha Chikumbutso chikhazikitsidwa ndi atumwi 11

Mateyu 26:26-29

Maliko 14:22-25

Luka 22:19, 20, Luka 22:24-30

[1 Akorinto 11:23-25]

Yerusalemu

Aneneratu za kukanidwa ndi Petulo, ndi kubalalika kwa atumwi

Mateyu 26:31-35

Maliko 14:27-31

Luka 22:31-38

Yohane 13:31-38

Yerusalemu

Mthandizi, kukondana, chisautso, pemphero la Yesu

Yohane 14:1–17:26

Getsemane

Kuzunzika mumtima m’mundamo, kuperekedwa ndi kumangidwa kwa Yesu

Mateyu 26:30, 36-56

Maliko 14:26, 32-52

Luka 22:39-53

Yohane 18:1-12

Yerusalemu

Kuzengedwa mlandu ndi Anasi, Kayafa, Khoti Lalikulu la Ayuda. Petulo am’kana

Mateyu 26:57–27:1

Maliko 14:53–15:1

Luka 22:54-71

Yohane 18:13-27

Yerusalemu

Yudasi wom’perekayo adzimangirira

Mateyu 27:3-10

[Machitidwe 1:18,19]

Yerusalemu

Pamaso pa Pilato, kenako kwa Herode, n’kubwereranso kwa Pilato

Mateyu 27:2, 11-14

Maliko 15:1-5

Luka 23:1-12

Yohane 18:28-38

Yerusalemu

Aperekedwa kukaphedwa, Pilato atayesa kum’masula

Mateyu 27:15-30

Maliko 15:6-19

Luka 23:13-25

Yohane 18:39–19:16

(Cha m’ma3 koloko masana, Lachisanu)

Gologota, Yerusalemu

Imfa ya Yesu pamtengo wozunzikirapo, ndi zochitika zotsatira

Mateyu 27:31-56

Maliko 15:20-41

Luka 23:26-49

Yohane 19:16-30

Yerusalemu

Mtembo wa Yesu auchotsa pamtengo wozunzikirapo ndi kukauika

Mateyu 27:57-61

Maliko 15:42-47

Luka 23:50-56

Yohane 19:31-42

Nisani 15

Yerusalemu

Ansembe ndi Afarisi aika alonda pamanda

Mateyu 27:62-66

Nisani 16

Yerusalemu ndi madera apafupi

Kuuka kwa Yesu ndi zochitika za pa tsikulo

Mateyu 28:1-15

Maliko 16:1-8

Luka 24:1-49

Yohane 20:1-25

Yerusalemu, Galileya

Yesu Khristu aonekera kangapo

Mateyu 28:16-20

[1 Akorinto 15:5-7]

[Machitidwe 1:3-8]

Yohane 20:26–21:25

Iyari 25

Phiri la Maolivi, pafupi ndi Betaniya

Yesu akwera kumwamba, tsiku la 40 pambuyo pa kuuka kwake

[Machitidwe 1:9-12]

Luka 24:50-53

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena