Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w11 9/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2011
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2011
w11 9/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

September 15, 2011

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

October 24-30, 2011

Yehova Ndi Cholowa Changa

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 38, 6

October 31, 2011–November 6, 2011

Kodi Mukulola Yehova Kukhala Cholowa Chanu?

TSAMBA 11

NYIMBO ZOIMBA: 40, 26

November 7-13, 2011

Tiyeni Tithamange Mpikisano Mopirira

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 54, 24

November 14-20, 2011

‘Thamangani N’cholinga Choti Mukalandire Mphoto’

TSAMBA 20

NYIMBO ZOIMBA: 54, 55

November 21-27, 2011

Kodi Mumadziwika ndi Yehova?

TSAMBA 25

NYIMBO ZOIMBA: 16, 4

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 TSAMBA 7-15

Kodi Yehova anatanthauza chiyani pamene anauza Alevi kuti: ‘Ine ndine cholowa chako?’ (Num. 18:20) Kodi ndi Alevi okha amene anali ndi mwayi woti Yehova akhale cholowa chawo? Kodi Yehova akhoza kukhala cholowa chathu masiku ano? Ngati ndi choncho kodi zingatheke bwanji? Nkhani ziwirizi zifotokoza mmene Yehova angakhalire cholowa chathu.

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 TSAMBA 16-24

Nkhani ziwirizi zitithandiza kuona zimene tingachite kuti tithamange bwinobwino mpikisano n’kukalandira mphoto. Kodi n’chiyani chingatithandize ndiponso kutilimbikitsa pa mpikisanowu? Kodi ndi zinthu ziti zimene zingatisokoneze kapena kutikola zomwe tiyenera kupewa? Nanga n’chiyani chingatithandize kuti tithamange mpaka kufika pamzere womaliza?

NKHANI YOPHUNZIRA 5 TSAMBA 25-29

Yehova amadziwa ndiponso kuvomereza atumiki ake okhulupirika. Kodi tiyenera kukhala ndi makhalidwe ati kuti tikhalebe pa ubwenzi ndi Yehova? Nkhaniyi ithandiza aliyense wa ife kudzifufuza.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

3 Kuwerenga Baibulo Kwandilimbikitsa pa Moyo Wanga Wonse

30 Khalani Olimba Mtima Ngati Pinihasi

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena