Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/12 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 27

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 27
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 27
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 2/12 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa February 27

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 27

Nyimbo Na. 17 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 2 ndime 16-23 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yesaya 63-66 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 114

Mph. 10: Zilengezo. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chimene chili patsamba 4, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingayambitsire phunziro la Baibulo Loweruka loyambirira m’mwezi wa March.

Mph. 15: Thandizani Anthu Amene Sakhulupirira Baibulo. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 58 mpaka 62. Chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri.

Mph. 10: “Dzina la Mulungu Liyeretsedwe.” Mafunso ndi mayankho. Lengezani masiku a msonkhano wadera ngati akudziwika.

Nyimbo Na. 100 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena