Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/15 tsamba 4
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Zomwe Munganene Pogawira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 12/15 tsamba 4

Zitsanzo za Ulaliki

Nsanja ya Olonda January 1

“Kodi aliyense akanakhala kuti amatsatira mfundo iyi, bwenzi zinthu zili bwanji m’dzikoli? [Werengani Aheberi 13:18, ndipo yembekezerani ayankhe.] Baibulo limanena kuti tiyenera kuchita zinthu zonse moona mtima. Magazini iyi ikufotokoza zimene tingachite kuti tipewe chinyengo cha mtundu uliwonse.”

Galamukani! January

“Ndikufuna ndikupatseni Galamukani! ya mwezi uno. [M’patseni magaziniyo.] Taonani funso limene lili patsamba 2 komanso mayankho ake. Kodi inuyo mungayankhe bwanji funso ili? [Yembekezerani ayankhe.] Nkhani iyi ikufotokoza mfundo za m’Baibulo zimene zingatithandize kuti tizikhala osangalala.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena