Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 September tsamba 2
  • September 4-10

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 4-10
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 September tsamba 2

September 4-10

Ezekieli 42-45

  • Nyimbo Na. 26 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kulambira Koyera Kunabwezeretsedwa”: (10 min.)

    • Ezek. 43:10-12​—Masomphenya a Ezekieli okhudza kachisi anathandiza Ayuda omwe anali ku ukapolo kuti alape komanso anawatsimikizira kuti kulambira koyera kudzabwezeretsedwa pamalo ake okwezeka (w99 3/1 8 ¶3; it-2 1082 ¶2)

    • Ezek. 44:23​—Ansembe ankafunika kuphunzitsa anthu kuti adziwe “kusiyana kwa chinthu chodetsedwa ndi choyera”

    • Ezek. 45:16​—Anthu ankayenera kuthandiza atsogoleri amene Yehova anawasankha kuti aziwatsogolera (w99 3/1 10 ¶10)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Ezek. 43:8, 9​—Kodi Aisiraeli anadetsa bwanji dzina la Mulungu? (it-2 467 ¶4)

    • Ezek. 45:9, 10​—Kodi Yehova amafuna kuti anthu amene amamutumikira azichita chiyani nthawi zonse? (it-2 140)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 44:1-9

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kukonzekera Ulaliki wa Mwezi Uno: (15 min.) Kukambirana “Zitsanzo za Ulaliki.” Pambuyo poonetsa vidiyo ya chitsanzo cha ulaliki iliyonse, kambiranani mfundo zikuluzikulu za m’vidiyoyo.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 143

  • “N’chifukwa Chiyani Mumaona Kuti Kulambira Koyera N’kofunika?”: (15 min.) Nkhani yokambirana.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu  6 ¶8-15 komanso tsamba 63

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 115 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena