Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 2/13 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2013
  • Nkhani Yofanana
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
Onani Zambiri
Galamukani!—2013
g 2/13 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

NKHANI YA PACHIKUTO: KODI OSAMUKIRA KUDZIKO LINA AMAKAPEZADI ZIMENE AKUFUNA? Tsamba 6 Mpaka 9

3 Zochitika Padzikoli

4 Mfundo Zothandiza Mabanja

Zimene Mungachite Kuti Musamakangane

10 Kucheza ndi Anthu

Katswiri Wopanga Maloboti Akufotokoza za Chikhulupiriro Chake

12 Zithunzi Zakale

Plato

14 Zimene Baibulo Limanena

Anthu Ovutika

16 Kodi Zinangochitika Zokha?

Mchira wa Gulo

MUNGAPEZE ZAMBIRI PA WEBUSAITI YA

www.jw.org

ACHINYAMATA

ZIMENE ACHINYAMATA AMADZIFUNSA

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Mameseji a Pafoni?

Mameseji amathandiza kwambiri kuti anthu azilankhulana. Koma ngati agwiritsidwa ntchito molakwika, akhoza kuwononga mbiri yanu komanso kuchititsa kuti anthu asamacheze nanu. Pezani malangizo okhudza anthu amene muyenera kumalemberana nawo mameseji, nkhani zake komanso nthawi yoyenera kulemberana mamesejiwo.

(Fufuzani pa mutu wakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA/ACHINYAMATA)

ANA

Werengani limodzi ndi ana anu nkhani za m’Baibulo zofotokozedwa pogwiritsa ntchito zithunzi. Kenako gwiritsani ntchito masamba omwe ali ndi zoti muchite ndi ana powathandiza kudziwa za anthu ofotokozedwa m’Baibulo komanso makhalidwe abwino.

(Fufuzani pa mutu wakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA/ANA)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena