Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/00 tsamba 2
  • Changu Chimene Chimautsa Ochuluka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Changu Chimene Chimautsa Ochuluka
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2000
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mutsanzira Kudzipereka kwa Yehova ndi Yesu pa Nyengo ya Chikumbutso Ikubwerayi?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Apainiya Othandiza 3,000 Akufunika
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1997
  • Cholinga Chabwino Kwambiri M’chaka Chautumiki Chatsopano
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
  • Nyengo ya Chikumbutso ndi Nthawi Yochita Zambiri
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2005
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2000
km 4/00 tsamba 2

Changu Chimene Chimautsa Ochuluka

Mtumwi Paulo anayamikira Akorinto chifukwa chakuti changu chawo pantchito yabwino ‘chinautsa [Akristu anzawo] ochuluka’. (2 Akor. 9:2) Kaŵirikaŵiri, munthu m’modzi, banja, gulu la phunziro la buku, kapena mpingo wonse ungachite zofananazo mwachangu chimene ali nacho mu ntchito yolalikira. Nazi njira zina zimene mungasonyezere changu pa utumiki.

◼ Patulani Loŵeruka kukhala Tsiku logaŵira Magazini.

◼ Chitani nawo mbali ina ya Utumiki wakumunda pamasiku a Lamlungu.

◼ Gwiritsani ntchito maola akumadzulo kuchita umboni wamadzulo.

◼ Chitani nawo maulaliki apadera alionse amene akonzedwa.

◼ Gwiritsani ntchito masiku a maholide akuntchito kapena akusukulu kupita muulaliki.

◼ Chirikizani utumiki nthaŵi ya woyendera dera.

◼ Chitani upainiya wothandiza mwezi umodzi kapena kuposerapo pachaka.

◼ Sinthani zochita zanu kuti muchite upainiya wokhazikika ngati n’kotheka.

Onani 2000 Yearbook of Jehovah’s Witnesses, masamba 17-19.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena