Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 September tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • NSANJA YA OLONDA
  • NSANJA YA OLONDA (tsamba lomaliza)
  • KUPHUNZITSA CHOONADI
  • LEMBANI ULALIKI WANUWANU
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 September tsamba 1
Akulalikira kwa mayi ndi mwana wake ku West Bengal m’dziko la India

Akulalikira kwa mayi ndi mwana wake ku West Bengal m’dziko la India

Zitsanzo za Ulaliki

NSANJA YA OLONDA

Nsanja ya Olonda, Na. 5 | Kodi Ndi Ndani Angatithandize Tikakhala pa Mavuto?

Funso: Tonsefe timafunika kuthandizidwa tikakumana ndi mavuto. Koma kodi ndi ndani angatithandize tikakhala pamavuto?

Lemba: 2 Akor. 1:3, 4

Perekani Magaziniyo: Maganiziyi ikufotokoza zimene Mulungu amachita kuti atithandize tikakumana ndi mavuto.

NSANJA YA OLONDA (tsamba lomaliza)

Funso: Anthu ena amaganiza kuti Ufumu wa Mulungu uli mumtima mwa munthu, pomwe ena amaganiza kuti Ufumu wa Mulungu udzakhalapo anthu akadzakwanitsa kukhazikitsa mtendere ndiponso mgwirizano padzikoli. Inuyo mukuganiza bwanji?

Lemba: Dan. 2:44

Perekani Magaziniyo: Lembali likusonyeza kuti Ufumu wa Mulungu ndi boma lenileni. Nkhaniyi ikufotokozanso zinthu zina zimene Baibulo limanena zokhudza Ufumu wa Mulungu

KUPHUNZITSA CHOONADI

Baibulo lotsegula

Funso: Kodi tingadziwe bwanji kuti Mulungu amatiganizira?

Lemba: 1 Pet. 5:7

Zoona Zake: Yehova amatiganizira, n’chifukwa chake amatiuza kuti tizipemphera kwa iye.

LEMBANI ULALIKI WANUWANU

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena