Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 January tsamba 2
  • Yehova Amasamalira Anthu Ake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amasamalira Anthu Ake
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Apambana Nkhondo Yolimbana ndi Masoka
    Galamukani!—1995
  • Munthu Aliyense Adzakhala Nacho Chakudya Chosakayikitsa
    Galamukani!—2002
  • Muzikhala Okonzeka Kuphunzira Zinthu Zatsopano
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Chakudya Chokwanira kwa Onse!
    Galamukani!—1995
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 January tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YESAYA 24-28

Yehova Amasamalira Anthu Ake

Yehova ndi wowolowa manja ndipo amatipatsa chakudya chambiri chauzimu.

Anthu akudyera limodzi chakudya

‘Yehova wa makamu adzakonzera anthu a mitundu yonse phwando’

25:6

  • Kale, kudyera limodzi chakudya kunkasonyeza kuti anthuwo ndi ogwirizana komanso okondana

“La zakudya zabwinozabwino zokhala ndi mafuta a m’mafupa, ndiponso la vinyo wokoma kwambiri, wosefedwa bwino”

  • Zakudya zabwinozabwino ndiponso vinyo wokoma kwambiri komanso wosefedwa bwino zikuimira chakudya chauzimu chabwino kwambiri chimene Yehova amatipatsa

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena