Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 September tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • NSANJA YA OLONDA
  • KUPHUNZITSA CHOONADI
  • KAPEPALA KOITANIRA ANTHU KUMISONKHANO (inv)
  • LEMBANI ULALIKI WANUWANU
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 September tsamba 1
A Mboni za Yehova akuitanira bambo wina kumisonkhano ya mpingo

Akuitanira anthu kumisonkhano ku Cook Islands

Zitsanzo za Ulaliki

NSANJA YA OLONDA

Nsanja ya Olonda Na. 5 2017 | N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kudziwa Zambiri Zokhudza Angelo?

Funso: Kodi angelo alipodi?

Lemba: Sal. 103:20

Perekani Magaziniyo: Nsanja ya Olonda iyi ikufotokoza zimene Baibulo limanena zokhudza angelo ndiponso mmene amatithandizira masiku ano.

KUPHUNZITSA CHOONADI

Baibulo lotsegula

Funso: Kodi mumaona kuti sayansi imatsutsana ndi Baibulo?

Lemba: Yes. 40:22

Zoona Zake: Zimene Baibulo limanena pa nkhani za sayansi n’zolondola.

KAPEPALA KOITANIRA ANTHU KUMISONKHANO (inv)

Kapepala Koitanira Anthu Kumisonkhano

Munganene Kuti: Ndikukuitanirani kumisonkhano yathu kuti mudzamvetsere nkhani yochokera m’Baibulo. Idzakambidwa ku Nyumba ya Ufumu omwe ndi malo athu olambirira. [Perekani kapepalako ndipo musonyezeni nthawi komanso malo a misonkhanoyo. Muuzeninso mutu wa nkhani ya mlungu umenewo.]

Funso: Kodi munayamba mwapitapo ku Nyumba ya Ufumu? [Ngati n’zotheka muonetseni vidiyo yakuti Kodi pa Nyumba ya Ufumu Pamachitika Zotani?]

LEMBANI ULALIKI WANUWANU

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena