Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 January tsamba 10
  • Kodi Mungatani Kuti Yehova Azikudalitsani?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungatani Kuti Yehova Azikudalitsani?
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amafuna Kuti Anthu Ake Azikhala Osiyana ndi Ena
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kukhala Okhutira Komanso Odzichepetsa?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Zikondwerero Zomwe Zimatikhudza
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Chaka cha Ufulu Komanso Ufulu Womwe Tidzakhale Nawo M’tsogolo
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 January tsamba 10

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kodi Mungatani Kuti Yehova Azikudalitsani?

Musamalambire milungu yopanda pake (Le 26:1; w08 4/15 4 ¶8)

Muzilambira Yehova m’njira imene amavomereza (Le 26:2; it-1 223 ¶3)

Muzimvera malamulo ake (Le 26:​3, 12; w91 3/1 17 ¶10)

Aisiraeli amene ankayesetsa kumvera malamulo a Yehova, ankakhala naye pa mtendere komanso ankapeza madalitso ambiri.

Mwamuna ndi mkazi wake akulalikira mosangalala pamalo opezeka anthu ambiri, pomwe anthu ena akudutsa kuchokera kogula zinthu ndipo ena akuyendera galimoto yodula.

Pa zinthu zotsatirazi, ndi ziti zimene mukusangalala nazo chifukwa chodalitsidwa ndi Yehova?

  • Kudziwa choonadi cha m’Baibulo

  • Kukhala ndi mtendere wamumtima

  • Kukhala ndi banja losangalala

  • Kukhala ndi chiyembekezo chabwino

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena