Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 M’malo anu onse okhala,+ mizinda idzawonongedwa+ ndipo malo okwezeka adzasakazidwa kuti akhale mabwinja ndiponso kuti maguwa anu ansembe akhale osakazidwa.+ Chotero maguwa anu ansembewo adzaphwanyidwa+ ndipo mafano anu onyansa sadzakhalaponso.+ Maguwa anu ofukizirapo zonunkhira adzagwetsedwa+ ndipo ntchito za manja anu zidzafafanizidwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena