Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/15 tsamba 3
  • Bokosi la Mafunso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Bokosi la Mafunso
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki​—Kusiya Kuphunzira ndi Munthu Yemwe Sakupita Patsogolo
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Kulangiza Molimba Mtima
    Muzikonda Anthu—Muziwaphunzitsa
  • Athandizeni Kuti ‘Akhazikike M’chikhulupiriro’
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • ‘Perekani Moyo Wanu’ kwa Ophunzira Anu
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 12/15 tsamba 3

Bokosi la Mafunso

◼ Kodi N’chiyani Chingatichititse Kusiya Kuphunzira Baibulo ndi Munthu?

Ngati munthu sakusintha ngakhale kuti taphunzira naye kwa nthawi yaitali, tiyenera kumusiya koma tizichita zimenezi mosamala. (Mat. 10:11) Tiyenera kudzifunsa kuti: Kodi tikapangana tsiku loti tiphunzire naye amapezeka? Kodi amakonzekereratu phunzirolo? Kodi anafikapo ku misonkhano ya mpingo? Kodi amauza anzake zimene akuphunzirazo? Kodi akusintha moyo wake chifukwa chotsatira mfundo za m’Baibulo? Poyankha mafunsowa, tiyenera kuganiziranso msinkhu wake komanso zimene angakwanitse kuchita chifukwa anthu sachita zinthu mofanana. Ngakhale titasiya kuphunzira naye, tiyenera kumuthandiza kudziwa kuti titha kudzapitiriza m’tsogolo ngati angafune.—1 Tim. 2:4.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena