Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 12:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pambuyo pake, Abulamu anasamutsa hema wake kumeneko. Kuyambira pa nthawi imeneyi, iye ankangokhalira kumanga ndi kusamutsa msasa, kulowera ku Negebu.+

  • Genesis 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tsopano Abulahamu anasamutsa msasa wake+ n’kupita kudziko la Negebu. Kenako anakakhala monga mlendo ku Gerari+ pakati pa Kadesi+ ndi Shura.+

  • Numeri 13:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Atapita ku Negebu,+ anakafika ku Heburoni.+ Kumeneko anapezako Ahimani, Sesai ndi Talimai,+ mbadwa za Anaki.*+ Mzinda wa Heburoni+ unamangidwa zaka 7 mzinda wa Zowani+ wa ku Iguputo usanamangidwe.

  • Oweruza 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kenako ana a Yuda anatsika kukamenyana ndi Akanani okhala m’dera lamapiri, ku Negebu+ ndi ku Sefela.+

  • 2 Samueli 24:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako anafika kumzinda wa mpanda wolimba wa Turo+ ndiponso kumizinda yonse ya Ahivi+ ndi Akanani. Pamapeto pake anafika ku Beere-seba+ ku Negebu,+ m’dziko la Yuda.

  • Obadiya 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Iwo adzatenga dera la Negebu kukhala lawo, komanso adzatenga dera lamapiri la Esau,+ dera la Sefela ndi dera la Afilisiti.+ Iwo adzatenganso madera a Efuraimu+ ndi Samariya kukhala awo.+ Benjamini adzatenga dera la Giliyadi+ kukhala lake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena