-
Genesis 47:29Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
29 Tsopano nthawi inayandikira yakuti Isiraeli amwalire.+ Ndiye anaitana mwana wake Yosefe n’kumuuza kuti: “Ngati ungandikomere mtima, ika dzanja lako pansi pa ntchafu yanga.+ Ulumbire kuti udzandisonyeza kukoma mtima kosatha ndipo udzakhala wokhulupirika kwa ine.+ Chonde, usadzandiike m’manda ku Iguputo kuno.+
-