Deuteronomo 33:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Kwa Benjamini anati:+“Wokondedwa+ wa Yehova akhale m’chitetezo cha Mulungu,+Pamene akumutchinjiriza tsiku lonse,+Ndipo iye akhale pakati pa mapewa ake.”+ Oweruza 20:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Pakati pa anthu onsewa, panali anthu amanzere+ 700 osankhidwa mwapadera. Aliyense wa anthu amenewa anali wamaluli poponya miyala*+ ndipo sanali kuphonya. 1 Samueli 9:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 “Mawa nthawi ngati ino ndikutumizira munthu kuchokera kudera la Benjamini,+ ndipo udzam’dzoze+ kukhala mtsogoleri wa anthu anga Aisiraeli. Iye adzapulumutsa anthu anga m’manja mwa Afilisiti,+ chifukwa ndaona kusautsika kwawo ndipo ndamva kulira kwawo.”+
12 Kwa Benjamini anati:+“Wokondedwa+ wa Yehova akhale m’chitetezo cha Mulungu,+Pamene akumutchinjiriza tsiku lonse,+Ndipo iye akhale pakati pa mapewa ake.”+
16 Pakati pa anthu onsewa, panali anthu amanzere+ 700 osankhidwa mwapadera. Aliyense wa anthu amenewa anali wamaluli poponya miyala*+ ndipo sanali kuphonya.
16 “Mawa nthawi ngati ino ndikutumizira munthu kuchokera kudera la Benjamini,+ ndipo udzam’dzoze+ kukhala mtsogoleri wa anthu anga Aisiraeli. Iye adzapulumutsa anthu anga m’manja mwa Afilisiti,+ chifukwa ndaona kusautsika kwawo ndipo ndamva kulira kwawo.”+