Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 18:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Zela,+ Ha-elefi, Yebusi, kutanthauza Yerusalemu,+ Gibea,+ ndi Kiriyati. Mizinda 14 ndi midzi yake.

      Ichi chinali cholowa cha ana a Benjamini potsata mabanja awo.+

  • Oweruza 1:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ana a Benjamini sanapitikitse Ayebusi amene anali kukhala m’Yerusalemu,+ moti Ayebusiwo akukhalabe ndi ana a Benjamini m’Yerusalemu kufikira lero.+

  • 2 Samueli 5:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Davide anayamba kukhala m’malo okhala mumpanda wolimba kwambiri, ndipo anawatcha Mzinda wa Davide. Iye anayamba kumanga malo onsewo kuyambira ku Chimulu cha Dothi*+ mpaka mkati.

  • Salimo 125:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova wazungulira anthu ake+

      Ngati mmene mapiri azungulirira Yerusalemu,+

      Kuyambira tsopano mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena