Genesis 49:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 “Benjamini adzapitiriza kukhadzula ngati mmbulu.+ M’mawa adzadya nyama imene wagwira, ndipo madzulo adzagawa zimene wafunkha.”+ 1 Samueli 17:40 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 40 Ndiyeno anatenga ndodo m’manja mwake ndi kusankha miyala isanu yosalala kwambiri ya m’chigwa.* Iye anaika miyalayi m’chikwama chake cha kubusa mmene anali kusungiramo zinthu, ndipo m’manja mwake munali gulaye.*+ Kenako anayamba kupita kumene kunali Mfilisiti uja. 1 Samueli 17:49 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 49 Pamenepo Davide anapisa dzanja m’chikwama chake ndi kutengamo mwala. Kenako anauponya ndi gulaye moti unamenya+ Mfilisiti uja pamphumi n’kuloweratu m’mutu mwake, ndipo anagwa pansi chafufumimba.+ 1 Mbiri 12:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Amuna onyamula mauta amenewa, ankatha kugwiritsa ntchito mkono wamanja ndi wamanzere+ kuponyera miyala+ kapena kuponyera mivi+ pa uta.+ Amenewa anali abale ake a Sauli wa fuko la Benjamini. 2 Mbiri 26:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Uziya anapitiriza kukonzera gulu lankhondo lonselo zishango,+ mikondo ing’onoing’ono,+ zisoti,+ zovala za mamba achitsulo,+ mauta,+ ndi miyala yoponya ndi gulaye.*+
27 “Benjamini adzapitiriza kukhadzula ngati mmbulu.+ M’mawa adzadya nyama imene wagwira, ndipo madzulo adzagawa zimene wafunkha.”+
40 Ndiyeno anatenga ndodo m’manja mwake ndi kusankha miyala isanu yosalala kwambiri ya m’chigwa.* Iye anaika miyalayi m’chikwama chake cha kubusa mmene anali kusungiramo zinthu, ndipo m’manja mwake munali gulaye.*+ Kenako anayamba kupita kumene kunali Mfilisiti uja.
49 Pamenepo Davide anapisa dzanja m’chikwama chake ndi kutengamo mwala. Kenako anauponya ndi gulaye moti unamenya+ Mfilisiti uja pamphumi n’kuloweratu m’mutu mwake, ndipo anagwa pansi chafufumimba.+
2 Amuna onyamula mauta amenewa, ankatha kugwiritsa ntchito mkono wamanja ndi wamanzere+ kuponyera miyala+ kapena kuponyera mivi+ pa uta.+ Amenewa anali abale ake a Sauli wa fuko la Benjamini.
14 Uziya anapitiriza kukonzera gulu lankhondo lonselo zishango,+ mikondo ing’onoing’ono,+ zisoti,+ zovala za mamba achitsulo,+ mauta,+ ndi miyala yoponya ndi gulaye.*+