Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamenepo ana a Isiraeli anayamba kufuulira Yehova kuti awathandize.+ Choncho Yehova anawapatsa mpulumutsi, Ehudi,+ munthu wogwiritsa ntchito dzanja lamanzere,+ wa fuko la Benjamini,+ mwana wa Gera. M’kupita kwa nthawi, ana a Isiraeli anatumiza msonkho wawo kwa Egiloni mfumu ya Mowabu, kudzera mwa Ehudi.

  • Oweruza 20:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pakati pa anthu onsewa, panali anthu amanzere+ 700 osankhidwa mwapadera. Aliyense wa anthu amenewa anali wamaluli poponya miyala*+ ndipo sanali kuphonya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena