Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 78:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Anapereka zokolola zawo kwa mphemvu,

      Ndipo ntchito yawo yolemetsa anaipereka kwa dzombe.+

  • Salimo 105:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Analamula kuti pagwe dzombe,+

      Ndipo panagwa dzombe losawerengeka la mtundu winawake.+

  • Miyambo 30:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Dzombe+ lilibe mfumu koma limauluka lonse litagawikana m’magulumagulu.+

  • Yoweli 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Zinthu zimene mbozi zinasiya zinadyedwa ndi dzombe.+ Zimene dzombelo linasiya zinadyedwa ndi ana a dzombe oyenda pansi opanda mapiko ndipo zimene ana a dzombe oyenda pansiwo anasiya zinadyedwa ndi mphemvu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena