Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma anthu onse amene aona ulemerero wanga,+ ndi zizindikiro zanga+ zimene ndinachita ku Iguputo, ndi zimene ndachita m’chipululu, amene akupitirizabe kundiyesa+ maulendo 10 onsewa, amenenso sanamvere mawu anga,+

  • Salimo 78:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Iwo anapitiriza kuyesa Mulungu m’mitima yawo+

      Mwa kupempha chakudya china chimene mtima wawo unalakalaka.+

  • Salimo 95:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pamene makolo anu anandiyesa.+

      Iwo anandisanthula, ndipo anaonanso ntchito zanga.+

  • Salimo 106:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Anasonyeza chikhumbo chawo chadyera m’chipululu,+

      Ndipo anayesa Mulungu m’chipululumo.+

  • Luka 4:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Poyankha Yesu anamuuza kuti: “Pajatu Malemba amati, ‘Usamuyese, Yehova Mulungu wako.’”+

  • 1 Akorinto 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kapena tisamuyese Yehova,+ mmene ena mwa iwo anamuyesera,+ n’kuwonongeka polumidwa ndi njoka.+

  • Aheberi 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 M’chipululumo, makolo anu anandiyesa ndi mayesero, ngakhale kuti anali ataona ntchito zanga+ kwa zaka 40.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena