Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 7:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 ineyo ndidzakuchotsani padziko langa limene ndakupatsani+ ndipo nyumba iyi yomwe ndaiyeretsa+ chifukwa cha dzina langa, ndidzaichotsa pamaso panga.+ Ndidzachititsa anthu kuipekera mwambi+ ndi kuitonza pakati pa mitundu yonse ya anthu.+

  • Salimo 24:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Dziko lapansi ndi zonse zili mmenemo ndi za Yehova,+

      Nthaka ndi yake pamodzi ndi onse okhala panthakapo.+

  • Salimo 85:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 85 Inu Yehova, mwasangalala ndi dziko lanu.+

      Mwabwezeretsa ana a Yakobo amene anagwidwa ndi kutengedwa kupita kudziko lina.+

  • Yoweli 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno Yehova adzachitira nsanje dziko lake+ ndipo adzamvera chifundo anthu ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena