Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Adzalefuka ndi njala+ ndi kuwonongeka ndi matenda otentha thupi koopsa,+

      Ndi chiwonongeko chowawa.+

      Ndidzawatumizira zilombo za mano ataliatali,+

      Pamodzi ndi njoka zapoizoni za m’fumbi.+

  • 2 Mafumu 17:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Atayamba kukhala mmenemo, iwo sanaope+ Yehova. Choncho Yehova anatumiza mikango+ pakati pawo ndipo inapha ena a iwo.

  • Yeremiya 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “‘Ndidzawagwetsera masoka a mitundu inayi,’+ watero Yehova. ‘Ndidzawatumizira lupanga kuti liwaphe, agalu kuti akoke mitembo yawo, zolengedwa zouluka zam’mlengalenga+ ndi zilombo zakutchire kuti ziwadye ndi kuwawononga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena