Deuteronomo 32:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Adzalefuka ndi njala+ ndi kuwonongeka ndi matenda otentha thupi koopsa,+Ndi chiwonongeko chowawa.+Ndidzawatumizira zilombo za mano ataliatali,+Pamodzi ndi njoka zapoizoni za m’fumbi.+ 2 Mafumu 17:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Atayamba kukhala mmenemo, iwo sanaope+ Yehova. Choncho Yehova anatumiza mikango+ pakati pawo ndipo inapha ena a iwo. Yeremiya 15:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 “‘Ndidzawagwetsera masoka a mitundu inayi,’+ watero Yehova. ‘Ndidzawatumizira lupanga kuti liwaphe, agalu kuti akoke mitembo yawo, zolengedwa zouluka zam’mlengalenga+ ndi zilombo zakutchire kuti ziwadye ndi kuwawononga.
24 Adzalefuka ndi njala+ ndi kuwonongeka ndi matenda otentha thupi koopsa,+Ndi chiwonongeko chowawa.+Ndidzawatumizira zilombo za mano ataliatali,+Pamodzi ndi njoka zapoizoni za m’fumbi.+
25 Atayamba kukhala mmenemo, iwo sanaope+ Yehova. Choncho Yehova anatumiza mikango+ pakati pawo ndipo inapha ena a iwo.
3 “‘Ndidzawagwetsera masoka a mitundu inayi,’+ watero Yehova. ‘Ndidzawatumizira lupanga kuti liwaphe, agalu kuti akoke mitembo yawo, zolengedwa zouluka zam’mlengalenga+ ndi zilombo zakutchire kuti ziwadye ndi kuwawononga.