Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 5:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 M’masiku a Samagara+ mwana wa Anati,

      M’masiku a Yaeli,+ m’njira munalibe odutsamo,

      Ndipo oyenda m’misewu anayamba kuyenda njira zolambalala.+

  • Yesaya 33:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Misewu ikuluikulu yawonongeka.+ Palibenso munthu woyenda m’njira.+ Iye waphwanya pangano+ ndipo wanyansidwa ndi mizinda.+ Sasamala za munthu aliyense.+

  • Ezekieli 14:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “‘Nditati ndichititse zilombo zolusa zakutchire kudutsa m’dzikolo,+ zilombozo n’kuliphera ana dzikolo,+ moti dzikolo n’kukhala bwinja lokhalokha popanda munthu aliyense wodutsamo chifukwa cha zilombo zolusazo,+

  • Zekariya 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 ‘Chotero ndinawabalalitsira ku mitundu yonse ya anthu+ imene sanali kuidziwa,+ ngati kuti atengedwa ndi mphepo yamkuntho. Dzikoli analisiya labwinja, popanda munthu wodutsamo kapena kuyendayendamo.+ Iwo anasandutsa dziko losiririka+ kukhala chinthu chodabwitsa.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena