Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “‘Ngati mukupereka nsembe yambewu yophika m’chiwaya,+ izikhala ya ufa wabwino kwambiri wothira mafuta, yopanda chofufumitsa.

  • Levitiko 6:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Nsembeyo ikhale yosakaniza ndi mafuta, yophika m’chiwaya.+ Ikhale yosakaniza bwino ndi mafuta. Upereke mitanda ya nsembe yambewu monga fungo lokhazika mtima pansi kwa Yehova.

  • 1 Mbiri 23:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Anali kutumidwanso pa ntchito zokhudza mkate wosanjikiza,+ ufa wosalala+ wa nsembe yambewu, mikate yopyapyala+ yopanda chofufumitsa,+ makeke ophika m’chiwaya,+ ufa wokanya wosakaniza ndi mafuta,+ ndiponso miyezo yosiyanasiyana.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena