Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “‘Ngati akupereka nsembe yachiyanjano+ kwa Yehova, ndipo akufuna kupereka ng’ombe yamphongo kapena yaikazi, azipereka yopanda chilema.+

  • Levitiko 7:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “‘Munthu amene wadya nyama ya nsembe yachiyanjano, imene ndi ya Yehova, pamene munthuyo ali wodetsedwa, aziphedwa kuti asakhalenso pakati pa anthu amtundu wake.+

  • Levitiko 22:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “‘Munthu akafuna kupereka nsembe yachiyanjano+ kwa Yehova kuti akwaniritse lonjezo lake+ kapena kuti ikhale nsembe yaufulu, azipereka ng’ombe kapena nkhosa yopanda chilema, kuti Mulungu ailandire. Izikhala yopanda chilema chilichonse.

  • 1 Akorinto 10:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kodi kapu+ ya dalitso imene timadalitsa, sitanthauza kugawana magazi a Khristu?+ Kodi mkate umene timanyema,+ sutanthauza kugawana thupi la Khristu?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena