Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 28:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 “Ndiyeno upange malaya odula manja ndi ulusi wabuluu wokhawokha, ovala mkati mwa efodi.+

  • Ekisodo 39:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndiyeno anapanga malaya odula manja+ ovala mkati mwa efodi, a nsalu yowomba ndi ulusi wabuluu wokhawokha.

  • Numeri 15:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 ‘Chingwecho chikhale ngati mphonje kwa inu, kuti mukachiyang’ana muzikumbukira malamulo onse+ a Yehova ndi kuwasunga. Muleke kutsatira zilakolako za mitima yanu ndi maso anu,+ chifukwa potsatira zilakolako zimenezo, mukuchita chiwerewere.+

  • Salimo 119:129
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 129 Zikumbutso zanu n’zodabwitsa.+

      N’chifukwa chake ine ndimazisunga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena