Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 28:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ndipo uveke Aroni m’bale wako pamodzi ndi ana ake zinthu zimenezi. Ukatero uwadzoze,+ uwapatse mphamvu*+ ndi kuwayeretsa, ndipo atumikire monga ansembe anga.

  • Levitiko 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Muzisunga malamulo anga.+ Ine ndine Yehova amene ndikukupatulani monga anthu oyera.+

  • 1 Akorinto 6:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndipo ena mwa inu munali otero.+ Koma mwasambitsidwa kukhala oyera,+ mwapatulidwa,+ mwayesedwa olungama+ m’dzina la Ambuye wathu Yesu Khristu,+ komanso ndi mzimu wa Mulungu wathu.+

  • Aheberi 9:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pakuti ngati magazi a mbuzi+ ndi a ng’ombe zamphongo+ komanso phulusa+ la ng’ombe yaikazi imene sinaberekepo, zimene amawaza nazo anthu oipitsidwa,+ zimawayeretsa mpaka kukhaladi oyera pamaso pa Mulungu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena