Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 22:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Chifukwa cha zimene mwachita ndidzakutamandani mumpingo waukulu.+

      Ndidzakwaniritsa malonjezo anga pamaso pa anthu oopa iye.+

  • Salimo 50:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pereka nsembe zoyamikira kwa Mulungu,+

      Ndipo pereka kwa Wam’mwambamwamba zimene walonjeza.+

  • Salimo 66:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndidzalowa m’nyumba yanu ndi nsembe zopsereza zathunthu.+

      Ine ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa inu+

  • Nahumu 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Taonani mapazi a munthu yemwe akuyenda pamwamba pa mapiri pobweretsa uthenga wabwino.+ Iye akulengeza za mtendere. Iwe Yuda, chita zikondwerero zako.+ Kwaniritsa zimene walonjeza+ chifukwa palibe munthu aliyense wopanda pake amene adzadutsa pakati pako.+ Munthu wopanda pakeyo adzaphedwa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena