Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Muwerenge kuyambira azaka 30+ mpaka 50,+ onse olowa m’gulu la ogwira ntchito+ m’chihema chokumanako.

  • Numeri 4:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Uwerenge kuyambira azaka 30 mpaka 50,+ onse olowa m’gulu la ogwira ntchito m’chihema chokumanako.

  • Numeri 4:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Uwerenge kuyambira azaka 30 mpaka 50, onse olowa m’gulu la ogwira ntchito pachihema chokumanako.+

  • Numeri 4:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Anawerenga kuyambira azaka 30+ mpaka 50,+ onse amene analowa m’gulu la ogwira ntchito m’chihema chokumanako.+

  • Numeri 4:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 kuyambira azaka 30 mpaka 50, onse amene analowa m’gulu la ogwira ntchito m’chihema chokumanako,+

  • Numeri 8:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Iye azingothandizira abale ake m’chihema chokumanako pochita utumiki wawo, koma asatumikire. Umu ndi mmene uzichitira ndi Alevi malinga ndi ntchito zawo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena