Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 4:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 kapena ngati wauzidwa kuti wachimwa mwa kuphwanya lamulo,+ azibweretsa mbuzi yaing’ono yamphongo,+ yopanda chilema, kuti ikhale nsembe yake.

  • Numeri 28:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Muziperekanso mwana wa mbuzi+ monga nsembe yamachimo kwa Yehova, kuwonjezera pa nsembe yopsereza ya tsiku ndi tsiku, limodzi ndi nsembe yake yachakumwa.+

  • 2 Mbiri 29:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Iwo anabweretsa ng’ombe zamphongo 7,+ nkhosa zamphongo 7, ana a nkhosa amphongo 7 ndi mbuzi zamphongo 7 kuti azipereke monga nsembe yamachimo+ ya ufumuwo, ya malo opatulika, ndi ya Yuda. Chotero Hezekiya anauza ana a Aroni, omwe anali ansembe,+ kuti apereke nsembeyo paguwa lansembe la Yehova.

  • Ezara 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamwambo wotsegulira nyumba ya Mulunguyo, anapereka nsembe ng’ombe zamphongo 100, nkhosa zamphongo 200, ndi ana a nkhosa amphongo 400. Anaperekanso mbuzi zamphongo 12 za nsembe ya machimo ya ana onse a Isiraeli mogwirizana ndi chiwerengero cha mafuko a Isiraeli.+

  • Ezara 8:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Anthu amene anabwera kuchokera ku ukapolo,+ amene kale anali m’dziko la eni, anapereka nsembe zopsereza+ kwa Mulungu wa Isiraeli. Anapereka ng’ombe zamphongo 12+ za Aisiraeli onse, nkhosa zamphongo 96,+ ana a nkhosa amphongo 77, ndi mbuzi zamphongo 12+ monga nsembe yamachimo. Zonsezi anazipereka monga nsembe yopsereza kwa Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena