Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 31:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Zofunkhazo muzigawe pawiri. Hafu iperekedwe kwa asilikali omwe anapita kunkhondo, ndipo hafu inayo iperekedwe kwa khamu la anthuwo.+

  • 1 Samueli 30:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndani angamve zimene mukunenazo? Pakuti gawo limene munthu amene anapita kunkhondo alandire, likhala lofanana ndi gawo limene munthu amene anali kulondera katundu alandire.+ Aliyense alandirapo kenakake.”+

  • Salimo 68:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mafumu enieniwo okhala ndi magulu a asilikali amathawa, ndithu amathawadi.+

      Mkazi wongokhala pakhomo, nayenso amagwira nawo ntchito yofunkha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena