-
Yesaya 30:17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
17 Anthu 1,000 adzanjenjemera chifukwa cha mawu oopseza a munthu mmodzi.+ Ndipo chifukwa cha mawu oopseza a anthu asanu, inuyo mudzathawa mpaka mudzatsala ochepa ngati mtengo wautali wa pangalawa wozikidwa pamwamba pa phiri, ndiponso ngati mtengo wozikidwa pamwamba pa phiri laling’ono kuti ukhale chizindikiro.+
-