Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Koma iwe Yuda,+ abale ako adzakutamanda.+ Dzanja lako lidzakhala pambuyo pa khosi la adani ako.+ Ana a bambo ako adzakugwadira.+

  • Deuteronomo 33:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Popitiriza, iye anapereka dalitso lotsatirali kwa Yuda,+ kuti:

      “Inu Yehova, imvani mawu a Yuda,+

      M’bweretseni kwa anthu ake.

      Manja ake amenya nkhondo pofuna kulanditsa zinthu zake.

      Mukhaletu mthandizi wake kwa adani ake.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena