Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 17:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Choncho iye anafunsa Davide kuti: “Kodi ine ndine galu+ kuti ubwere kwa ine ndi ndodo?” Atatero, anatemberera Davide m’dzina la milungu yake.+

  • 2 Samueli 16:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno Mfumu Davide inafika ku Bahurimu.+ Kumeneko inaona mwamuna wina wa m’banja la Sauli, dzina lake Simeyi,+ mwana wa Gera akutuluka ndipo anali kulankhula mawu onyoza.+

  • Salimo 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ngati mwakwiya, musachimwe.+

      Lankhulani mumtima mwanu, muli pabedi panu,+ ndipo mukhale chete. [Seʹlah.]

  • Salimo 39:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Ine ndinati: “Ndidzatchinjiriza njira zanga,+

      Kuti ndisachimwe ndi lilime langa.+

      Ndidzamanga pakamwa panga kuti patetezeke,+

      Nthawi zonse pamene woipa ali pamaso panga.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena