Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 38:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Tsopano Yuda anachoka pakati pa abale ake, ndipo anakamanga hema wake pafupi ndi munthu wina wachiadulamu,+ dzina lake Hira.

  • Yoswa 15:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Yarimuti,+ Adulamu,+ Soko,+ Azeka,+

  • 2 Samueli 23:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno pa nthawi yokolola, atatu mwa atsogoleri 30+ anapita kwa Davide kuphanga la Adulamu.+ Apa n’kuti Afilisiti atamanga msasa wa mahema m’chigwa cha Arefai.+

  • 1 Mbiri 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako, atatu mwa atsogoleri 30+ anapita kwa Davide kuthanthwe, kuphanga la Adulamu.+ Pa nthawiyi gulu lankhondo la Afilisiti linali litamanga msasa m’chigwa cha Arefai.+

  • Mika 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iwe mkazi wokhala ku Maresha+ ndidzakubweretsera wolanda zinthu za ena.+ Ulemerero wa Isiraeli udzafika ku Adulamu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena