Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Chinyengo chimakhala mumtima mwa anthu okonza chiwembu,+ koma olimbikitsa mtendere amasangalala.+

  • Miyambo 14:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Anthu okonza chiwembu amasochera,+ koma anthu okonzekera kuchita zabwino amapeza kukoma mtima kosatha ndi choonadi.+

  • Miyambo 16:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Iye amatsinzinira ndi maso ake pokonza ziwembu.+ Amalumirira mano, ndipo amakwanitsadi kuchita chiwembu.

  • Miyambo 24:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Aliyense wokonzera anzake ziwembu adzatchedwa katswiri wa maganizo oipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena