Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 21:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti akuchitirani zinthu zoipa.+

      Alinganiza kuchita zinthu zimene sangazikwanitse.+

  • Miyambo 6:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mumtima mwake muli zopotoka.+ Nthawi zonse amakhala akukonza zoipa.+ Amakhalira kuyambanitsa anthu.+

  • Miyambo 12:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Munthu wabwino Yehova amakondwera naye,+ koma munthu wamaganizo oipa iye amamutcha woipa.+

  • Aroma 1:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 ndi miseche.+ Anakhala odana ndi Mulungu, achipongwe,+ odzikweza,+ odzimva,+ oyambitsa zoipa,+ osamvera makolo,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena