Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 35:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Iwo salankhula mawu amtendere,+

      Koma amakonzera chiwembu anthu ofatsa a padziko lapansi,

      Kuti awachitire zachinyengo.+

  • Salimo 36:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ali pabedi lake amakonza chiwembu kuti apweteke anzake.+

      Amaima panjira yoipa.+

      Sapewa kuchita zinthu zoipa.+

  • Miyambo 6:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 mtima wokonzera ena ziwembu,+ mapazi othamangira kukachita zoipa,+

  • Yesaya 32:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Munthu wakhalidwe loipayo, njira zake n’zoipa.+ Iye amakonza zochita khalidwe lotayirira,+ n’cholinga choti apweteke anthu ozunzika pogwiritsa ntchito mawu abodza,+ ngakhale pamene munthu wosauka akunena zoona.

  • Mika 2:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Tsoka kwa anthu amene amati akagona pabedi, amakonza chiwembu ndiponso kuganiza mmene angachitire zoipa.+ M’mawa kukangocha, iwo amazichitadi+ chifukwa chakuti ali ndi mphamvu zochitira zimenezo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena